Al Haqq Magazine

Al Haqq Magazine

Share

29/11/2025

Funso

Kodi mayi yemwe anakwatiwapo ndipo mwamuna wake anamwalira kapena kusiyidwa chabe, pofuna kukwatiwatinso ndikofunika kuti awuze makolo ake za zimenezi monga anachitira pachiyambi pamene amakwatiwa ali mtsikana kapena palibe vuto ngakhale makolo atapanda kuwuzidwa?

Yankho

Tinene zoti makolo ayenera kukhudzidwa pakukwatiwa kwa mwana wake pofuna kutsatira malamulo aChisilamu omwe amafuna kuteteza miyoyo ya anthu, kusunga ulemerero, chikhulupiliro, chuma komanso kuganiza kwa munthu. Choncho makolo amafunika pokwatiwa pa mwana wake pofuna kulemekeza mwambo ofunikirawu. Ngakhale kuti mkazi yemwe anakwatiwapo atha kukwatiwanso popanda makolo, ndibwino kuti makolo asasiyidwe padera pamene mkazi kapena mamuna akufuna kukwatira. Kwenikweni izi zili choncho pofuna kuonetsetsa kuti mkazi asakhale ngati wangotoledwa panjira powonetsatsanso kuti pali umboni wokwanira.

22/10/2025

Click the link to download Al-Haqq October 2025.
https://bit.ly/4qBLOxQ

Want your business to be the top-listed Media Company in Limbe?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Address

Globe Chambers
Limbe
BOX497,BLANTYRE