Al Haqq Magazine
29/11/2025
Funso
Kodi mayi yemwe anakwatiwapo ndipo mwamuna wake anamwalira kapena kusiyidwa chabe, pofuna kukwatiwatinso ndikofunika kuti awuze makolo ake za zimenezi monga anachitira pachiyambi pamene amakwatiwa ali mtsikana kapena palibe vuto ngakhale makolo atapanda kuwuzidwa?
Yankho
Tinene zoti makolo ayenera kukhudzidwa pakukwatiwa kwa mwana wake pofuna kutsatira malamulo aChisilamu omwe amafuna kuteteza miyoyo ya anthu, kusunga ulemerero, chikhulupiliro, chuma komanso kuganiza kwa munthu. Choncho makolo amafunika pokwatiwa pa mwana wake pofuna kulemekeza mwambo ofunikirawu. Ngakhale kuti mkazi yemwe anakwatiwapo atha kukwatiwanso popanda makolo, ndibwino kuti makolo asasiyidwe padera pamene mkazi kapena mamuna akufuna kukwatira. Kwenikweni izi zili choncho pofuna kuonetsetsa kuti mkazi asakhale ngati wangotoledwa panjira powonetsatsanso kuti pali umboni wokwanira.
22/10/2025
Click the link to download Al-Haqq October 2025.
https://bit.ly/4qBLOxQ
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the business
Website
Address
Limbe
BOX497,BLANTYRE